Hoseya 6:5 - Buku Lopatulika5 Chifukwa chake ndawalikha mwa aneneri; ndawapha ndi mau a pakamwa panga; ndi maweruzo anga atuluka ngati kuunika. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20145 Chifukwa chake ndawalikha mwa aneneri; ndawapha ndi mau a pakamwa panga; ndi maweruzo anga atuluka ngati kuunika. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa5 Nchifukwa chake ndakuŵazani ngati nkhuni ndi machenjezo a aneneri, ndakuphani ndi mau anga. Chigamulo changa nchoonekeratu ngati kuŵala kwa dzuŵa. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero5 Choncho ndakuwazani ngati nkhuni kudzera mwa aneneri anga, ndakuphani ndi mawu a pakamwa panga; chigamulo changa chinangʼanima ngati mphenzi pa inu. Onani mutuwo |