Hoseya 6:6 - Buku Lopatulika6 Pakuti ndikondwera nacho chifundo, si nsembe ai; ndi kumdziwa Mulungu kuposa nsembe zopsereza. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20146 Pakuti ndikondwera nacho chifundo, si nsembe ai; ndi kumdziwa Mulungu kuposa nsembe zopsereza. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa6 Kunena zoona Ine ndimafuna chikondi chosasinthika, osati nsembe chabe. Ndifuna kuti anthu andidziŵe Ine Mulungu m'malo mwa kumangopereka nsembe zopsereza. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero6 Pakuti Ine ndimafuna chifundo osati nsembe, ndi kudziwa Mulungu kulekana ndi nsembe zopsereza. Onani mutuwo |