Hoseya 6:7 - Buku Lopatulika7 Koma iwo analakwira chipangano ngati Adamu, m'mene anandichitira monyenga. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20147 Koma iwo analakwira chipangano ngati Adamu, m'mene anandichitira monyenga. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa7 “Koma anthuwo adaphwanya chipangano changa monga adachitira Adamu. Potero, adandichitira zosakhulupirika. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero7 Monga Adamu, anthuwa aphwanya pangano langa, iwo sanakhulupirike kwa Ine. Onani mutuwo |