Hoseya 6:8 - Buku Lopatulika8 Giliyadi ndiwo mzinda wa ochita zoipa, wa mapazi a mwazi. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20148 Giliyadi ndiwo mudzi wa ochita zoipa, wa mapazi a mwazi. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa8 Giliyadi ndi mzinda wa anthu ochita zoipa, akungophana basi. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero8 Giliyadi ndi mzinda wa anthu ochita zoyipa, okhala ndi zizindikiro za kuphana. Onani mutuwo |
Ndiponso udziwa chimene Yowabu mwana wa Zeruya anandichitira, inde chimene anawachitira akazembe awiri aja a magulu a nkhondo a Israele, ndiwo Abinere mwana wa Nere, ndi Amasa mwana wa Yetere, amene aja anawapha, nakhetsa mwazi ngati wa nkhondo masiku a mtendere, napaka mwazi wa nkhondo pa lamba lake la m'chuuno mwake, ndi pa nsapato za pa mapazi ake.