Hoseya 6:9 - Buku Lopatulika9 Ndipo monga magulu a mbala alalira munthu, momwemo msonkhano wa ansembe amapha panjira ya ku Sekemu; indedi achita choipitsitsa. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20149 Ndipo monga magulu a mbala alalira munthu, momwemo msonkhano wa ansembe amapha pa njira ya ku Sekemu; indedi achita choipitsitsa. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa9 Monga mbala zimalalira munthu, momwemonso ansembe amasonkhana kuti azipha anthu pa njira ya ku Sekemu. Zoonadi amachita zachifwamba zambiri. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero9 Monga momwe mbala zimadikirira anthu, magulu a ansembe amachitanso motero; iwo amapha anthu pa njira yopita ku Sekemu, kupalamula milandu yochititsa manyazi. Onani mutuwo |