Marko 4:34 - Buku Lopatulika34 ndipo sanalankhule nao wopanda fanizo: koma m'tseri anatanthauzira zonse kwa ophunzira ake. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201434 ndipo sanalankhule nao wopanda fanizo: koma m'tseri anatanthauzira zonse kwa ophunzira ake. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa34 Sankaŵaphunzitsa popanda mafanizo. Koma ankati akakhala payekha ndi ophunzira ake, ankaŵatanthauzira zonse. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero34 Iye sananene kanthu kwa iwo osagwiritsa ntchito fanizo. Koma ali yekha ndi ophunzira ake, ankawatanthauzira zonse. Onani mutuwo |