Marko 4:35 - Buku Lopatulika35 Ndipo dzuwa lomwelo, pofika madzulo, ananena kwa iwo, Tiolokere tsidya lina. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201435 Ndipo dzuwa lomwelo, pofika madzulo, ananena kwa iwo, Tiolokere tsidya lina. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa35 Tsiku lomwelo, dzuŵa litaloŵa, Yesu adauza ophunzira ake kuti, “Tiyeni tiwoloke, tipite ku tsidya.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero35 Tsiku limenelo atafika madzulo, anawuza ophunzira ake kuti, “Tiyeni tiwolokere tsidya lina.” Onani mutuwo |