Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Marko 4:33 - Buku Lopatulika

33 Ndipo ndi mafanizo otere ambiri analankhula nao mau, monga anakhoza kumva;

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

33 Ndipo ndi mafanizo otere ambiri analankhula nao mau, monga anakhoza kumva;

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

33 Yesu ankaphunzitsa anthu ndi mafanizo ambiri onga ameneŵa, polinganiza ndi nzeru za anthuwo.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

33 Ndi mafanizo ambiri onga awa Yesu anayankhula mawu kwa iwo, monga mmene akanatha kumvetsa.

Onani mutuwo Koperani




Marko 4:33
7 Mawu Ofanana  

Ndipo Iye anawauzira zinthu zambiri m'mafanizo, nanena, Onani, wofesa anatuluka kukafesa mbeu.


koma pamene ifesedwa, imera nkukula koposa zitsamba zonse, nkukhala ndi nthambi zazikulu; kotero kuti mbalame za m'mlengalenga zikhoza kubindikira mumthunzi mwake.


ndipo sanalankhule nao wopanda fanizo: koma m'tseri anatanthauzira zonse kwa ophunzira ake.


Ndili nazo zambirinso zakunena kwa inu, koma simungathe kuzisenza tsopano lino.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa