Marko 4:10 - Buku Lopatulika10 Ndipo pamene anakhala pa yekha, iwo amene anali pafupi ndi Iye pamodzi ndi khumi ndi awiriwo anamfunsa za mafanizo. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201410 Ndipo pamene anakhala pa yekha, iwo amene anali pafupi ndi Iye pamodzi ndi khumi ndi awiriwo anamfunsa za mafanizo. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa10 Pamene Yesu anali payekha, ophunzira khumi ndi aŵiri aja pamodzi ndi enanso amene ankakhala naye adadzamufunsa za mafanizowo. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero10 Ali yekha, ophunzira ndi ena omuzungulira, anamufunsa za mafanizo. Onani mutuwo |