Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Amosi 2:3 - Buku Lopatulika

ndipo ndidzalikha woweruza pakati pake, ndi kupha akalonga ake onse, ati Yehova.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

ndipo ndidzalikha woweruza pakati pake, ndi kupha akalonga ake onse, ati Yehova.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Ndidzaŵaphera wolamulira wao, Ndidzaphanso nduna zake pamodzi naye.” Akuterotu Chauta.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Ndidzawononga wolamulira wake ndi kupha akuluakulu onse amene ali pamodzi ndi iye,” akutero Yehova.

Onani mutuwo



Amosi 2:3
10 Mawu Ofanana  

Atsanulira mnyozo pa akalonga, nawansezera olimba lamba lao.


Oweruza ao anagwetseka pambali pa thanthwe; nadzamva mau anga kuti ndiwo okondweretsa.


Tsono, mafumu inu, chitani mwanzeru; langikani, oweruza inu a dziko lapansi.


amene asandutsa akalonga kuti akhale achabe, nasandutsa oweruza a dziko lapansi akhale opanda pake.


Nyanga ya Mowabu yaduka, ndipo wathyoka mkono wake, ati Yehova.


Pakuti, chifukwa wakhulupirira ntchito zanu ndi chuma chanu, iwenso udzagwidwa; ndipo Kemosi adza kundende, ansembe ake ndi akulu ake pamodzi.


Pakuti ndidziwa kuti zolakwa zanu nzochuluka, ndi machimo anu ndi olimba, inu akusautsa olungama, akulandira chokometsera mlandu, akukankha osowa kuchipata.


inu osintha chiweruzo chikhale chivumulo, nimugwetsa pansi chilungamo.


Kodi akavalo adzathamanga pathanthwe? Kodi adzalimako ndi ng'ombe pakuti mwasanduliza chiweruzo chikhale ndulu, ndi chipatso cha chilungamo chikhale chivumulo;


Ndimuona, koma tsopano ai; ndimpenya, koma si pafupi ai; idzatuluka nyenyezi mu Yakobo, ndi ndodo yachifumu idzauka mu Israele, nidzakantha malire a Mowabu, nidzapasula ana onse a Seti.