Amosi 5:7 - Buku Lopatulika7 inu osintha chiweruzo chikhale chivumulo, nimugwetsa pansi chilungamo. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20147 inu osintha chiweruzo chikhale chivumulo, nimugwetsa pansi chilungamo. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa7 Tsoka kwa inu amene mumasandutsa chilungamo kuti chikhale choipa, inu amene mumanyoza zolungama. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero7 Inu amene mumasandutsa chiweruzo cholungama kukhala chowawa ndi kunyoza chilungamo. Onani mutuwo |
Koma wolungamayo akabwerera kuleka chilungamo chake, nakachita mphulupulu, ndi kuchita monga mwa zonyansa zonse azichita woipa, adzakhala ndi moyo kodi? Nnena chimodzi cha zolungama zake zonse adzazichita chidzakumbukika m'kulakwa kwake analakwa nako, ndi m'kuchimwa kwake anachimwa nako; momwemo adzafa.