Amosi 5:6 - Buku Lopatulika6 Funani Yehova, ndipo mudzakhala ndi moyo; angabuke ngati moto m'nyumba ya Yosefe, ndipo unganyeke wopanda wakuzima mu Betele; Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20146 Funani Yehova, ndipo mudzakhala ndi moyo; angabuke ngati moto m'nyumba ya Yosefe, ndipo unganyeke wopanda wakuzima m'Betele; Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa6 Muchite zimene Chauta afuna, kuti mukhalebe ndi moyo. Mukapanda kutero, adzatentha banja la Yosefe ngati moto, ndipo motowo udzapsereza a ku Betele popanda wina wouzimitsa. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero6 Funani Yehova kuti mukhale ndi moyo, mukapanda kutero Iye adzatentha nyumba ya Yosefe ngati moto; motowo udzawononga, ndipo sipadzakhala wina wozimitsa motowo ku Beteli. Onani mutuwo |