Yeremiya 48:25 - Buku Lopatulika25 Nyanga ya Mowabu yaduka, ndipo wathyoka mkono wake, ati Yehova. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201425 Nyanga ya Mowabu yaduka, ndipo wathyoka mkono wake, ati Yehova. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa25 Mphamvu za Mowabu zaonongeka, mkono wake wolimba wathyoka,” akutero Chauta. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero25 Mphamvu za Mowabu zawonongeka; mkono wake wathyoka,” akutero Yehova. Onani mutuwo |