Yeremiya 48:7 - Buku Lopatulika7 Pakuti, chifukwa wakhulupirira ntchito zanu ndi chuma chanu, iwenso udzagwidwa; ndipo Kemosi adza kundende, ansembe ake ndi akulu ake pamodzi. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20147 Pakuti, chifukwa wakhulupirira ntchito zanu ndi chuma chanu, iwenso udzagwidwa; ndipo Kemosi adza kundende, ansembe ake ndi akulu ake pamodzi. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa7 Inunso mudzagwidwa chifukwa choti munkadalira ntchito zanu ndi chuma chanu. Kemosi, mulungu wanu, adzatengedwa ukapolo, pamodzi ndi ansembe ake ndi akalonga ake. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero7 Popeza inu munkadalira ntchito zanu ndi chuma chanu, nanunso mudzatengedwa ukapolo, ndipo Kemosi adzapita ku ukapolo, pamodzi ndi ansembe ake ndi akuluakulu ake. Onani mutuwo |