Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




2 Samueli 22:23 - Buku Lopatulika

Pakuti maweruzo ake onse anali pamaso panga; ndipo za malemba ake, sindinawapatukire.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Pakuti maweruzo ake onse anali pamaso panga; ndipo za malemba ake, sindinawapatukira.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Ndidamvera malangizo ake onse, ndipo malamulo ake sindidaŵataye.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Malamulo ake onse ali pamaso panga, sindinasiye malangizo ake.

Onani mutuwo



2 Samueli 22:23
14 Mawu Ofanana  

Sindinapatukane nao maweruzo anu; pakuti Inu munandiphunzitsa.


Chifukwa chake ndiyesa ngolunjika malangizo anu onse akunena zonse; koma ndidana nazo njira zonse zonyenga.


Ndinafotokozera ndi milomo yanga maweruzo onse a pakamwa panu.


Ndinasankha njira yokhulupirika; ndinaika maweruzo anu pamaso panga.


Pamenepo sindidzachita manyazi, pakupenyerera malamulo anu onse.


Malamulo anu onse ngokhulupirika; andilondola nalo bodza; ndithandizeni.


Ndipo onse awiri anali olungama mtima pamaso pa Mulungu, namayendabe m'malamulo onse ndi zoikika za Ambuye osachimwa.


Muli abwenzi anga inu, ngati muzichita zimene ndikulamulani inu.


kuti mtima wake usadzikuze pa abale ake, ndi kuti asapatukire lamulolo, kulamanja kapena kulamanzere; kuti achuluke masiku ake, mu ufumu wake, iye ndi ana ake pakati pa Israele.


Ndipo kudzakhala, chifukwa cha kumvera inu maweruzo awa, ndi kuwasunga, ndi kuwachita, Yehova Mulungu wanu adzakusungirani chipangano ndi chifundo chimene analumbirira makolo anu;


Chenjerani mungaiwale Yehova Mulungu wanu, ndi kusasunga malamulo ake, ndi maweruzo ake, ndi malemba ake, amene ndikuuzani lero lino;