Masalimo 119:86 - Buku Lopatulika86 Malamulo anu onse ngokhulupirika; andilondola nalo bodza; ndithandizeni. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201486 Malamulo anu onse ngokhulupirika; andilondola nalo bodza; ndithandizeni. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa86 Malamulo anu onse ndi osasinthika. Anthuwo amandizunza ndi mabodza ao; thandizeni! Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero86 Malamulo anu onse ndi odalirika; thandizeni, pakuti anthu akundizunza popanda chifukwa. Onani mutuwo |