Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Masalimo 119:86 - Buku Lopatulika

86 Malamulo anu onse ngokhulupirika; andilondola nalo bodza; ndithandizeni.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

86 Malamulo anu onse ngokhulupirika; andilondola nalo bodza; ndithandizeni.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

86 Malamulo anu onse ndi osasinthika. Anthuwo amandizunza ndi mabodza ao; thandizeni!

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

86 Malamulo anu onse ndi odalirika; thandizeni, pakuti anthu akundizunza popanda chifukwa.

Onani mutuwo Koperani




Masalimo 119:86
17 Mawu Ofanana  

Ndithandizeni Yehova, Mulungu wanga: Ndipulumutseni monga mwa chifundo chanu;


Chifukwa chake ndiyesa ngolunjika malangizo anu onse akunena zonse; koma ndidana nazo njira zonse zonyenga.


Mboni zanuzo mudazilamulira zili zolungama ndi zokhulupirika ndithu.


Chilungamo chanu ndicho chilungamo chosatha; ndi chilamulo chanu ndicho choonadi.


Inu muli pafupi, Yehova; ndipo malamulo anu onse ndiwo choonadi.


Odzikuza achite manyazi, popeza anandichitira monyenga ndi bodza: Koma ine ndidzalingalira malangizo anu.


Mundilanditse kwa adani anga, Yehova; ndibisala mwa Inu.


Kuopa Yehova kuli mbee, kwakukhalabe nthawi zonse; maweruzo a Yehova ali oona, alungama konsekonse.


Adani anga asandikondwerere ine monyenga; okwiya nane kopanda chifukwa asanditsinzinire.


Pakuti ananditchera ukonde wao m'mbunamo kopanda chifukwa, anakumbira moyo wanga dzenje kopanda chifukwa.


Koma adani anga ali ndi moyo, nakhala ndi mphamvu, ndipo akundida kopanda chifukwa achuluka.


Koma ine ndine wozunzika ndi waumphawi; mundifulumirire, Mulungu. Inu ndinu mthandizi wanga ndi Mpulumutsi wanga; musachedwe, Yehova.


Kodi choipa chibwezedwe pa chabwino? Pakuti akumbira moyo wanga dzenje. Mukumbukire kuti ndinaima pamaso panu kuwanenera zabwino, kuwachotsera iwo ukali wanu.


Chotero chilamulo chili choyera, ndi chilangizo chake nchoyera, ndi cholungama, ndi chabwino.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa