Yohane 15:14 - Buku Lopatulika14 Muli abwenzi anga inu, ngati muzichita zimene ndikulamulani inu. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201414 Muli abwenzi anga inu, ngati muzichita zimene ndikulamulani inu. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa14 Inu ndinu abwenzi anga ngati muchita zimene ndikulamulani. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero14 Inu ndinu abwenzi anga ngati muchita zimene Ine ndikulamulani. Onani mutuwo |