Masalimo 119:128 - Buku Lopatulika128 Chifukwa chake ndiyesa ngolunjika malangizo anu onse akunena zonse; koma ndidana nazo njira zonse zonyenga. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 2014128 Chifukwa chake ndiyesa ngolunjika malangizo anu onse akunena zonse; koma ndidana nazo njira zonse zonyenga. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa128 Malamulo anu onse amalungamitsa mayendedwe anga. Ndimadana ndi njira iliyonse yonyenga. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero128 ndiponso chifukwa choti ndimaona kuti malangizo anu onse ndi wowongoka, ndimadana ndi njira iliyonse yoyipa. Onani mutuwo |