Masalimo 119:13 - Buku Lopatulika13 Ndinafotokozera ndi milomo yanga maweruzo onse a pakamwa panu. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201413 Ndinafotokozera ndi milomo yanga maweruzo onse a pakamwa panu. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa13 Ndimalalika ndi mau anga malangizo onse a pakamwa panu. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero13 Ndi milomo yanga ndimafotokoza malamulo anu onse amene amachokera pakamwa panu. Onani mutuwo |