Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Masalimo 119:13 - Buku Lopatulika

13 Ndinafotokozera ndi milomo yanga maweruzo onse a pakamwa panu.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

13 Ndinafotokozera ndi milomo yanga maweruzo onse a pakamwa panu.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

13 Ndimalalika ndi mau anga malangizo onse a pakamwa panu.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

13 Ndi milomo yanga ndimafotokoza malamulo anu onse amene amachokera pakamwa panu.

Onani mutuwo Koperani




Masalimo 119:13
14 Mawu Ofanana  

Sindidzafa koma ndidzakhala ndi moyo, ndipo ndidzafotokozera ntchito za Yehova.


Lilime langa liimbire mau anu; pakuti malamulo anu onse ndiwo olungama.


Ndidzalankhulanso za umboni wanu pamaso pa mafumu, osachitapo manyazi.


Pakuti maweruzo ake onse anali pamaso panga, ndipo malemba ake sindinawachotse kwa ine.


Idzani ananu ndimvereni ine, ndidzakulangizani zakumuopa Yehova.


Pakamwa pa wolungama palankhula zanzeru, ndi lilime lake linena chiweruzo.


ukasunge zolingalira, milomo yako ilabadire zomwe udziwa.


Chimene ndikuuzani inu mumdima, tachinenani poyera; ndi chimene muchimva m'khutu, muchilalikire pa matsindwi a nyumba.


Akubadwa inu a njoka, mungathe bwanji kulankhula zabwino, inu akukhala oipa? Pakuti m'kamwa mungolankhula mwa kusefuka kwake kwa mtima.


pakuti sitingathe ife kuleka kulankhula zimene tinaziona ndi kuzimva.


Ndipo mau awa ndikuuzani lero, azikhala pamtima panu;


ndipo muziwaphunzitsa mwachangu kwa ana anu, ndi kuwalankhula awa pokhala pansi m'nyumba zanu, ndi poyenda inu panjira, ndi pogona inu pansi, ndi pouka inu.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa