Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Yohane 6:3 - Buku Lopatulika

Koma Yesu anakwera kuphiri, nakhala pansi komweko pamodzi ndi ophunzira ake.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Koma Yesu anakwera kuphiri, nakhala pansi komweko pamodzi ndi ophunzira ake.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Yesu adakwera m'phiri nakhala pansi ndi ophunzira ake.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Kenaka Yesu anakwera pa phiri nakhala pansi ndi ophunzira ake.

Onani mutuwo



Yohane 6:3
7 Mawu Ofanana  

Ndipo pamene Iye anawauza makamuwo, anakwera m'phiri pa yekha, kukapemphera: ndipo pamene panali madzulo, Iye anakhala kumeneko yekha.


Ndipo Yesu anachoka kumeneko, nadza kunyanja ya Galileya, nakwera m'phiri, nakhala pansi pamenepo.


Ndipo m'mene Iye anaona makamu, anakwera m'phiri; ndipo m'mene Iye anakhala pansi, anadza kwa Iye ophunzira ake;


Ndipo anakwera m'phiri, nadziitanira iwo amene anawafuna Iye mwini; ndipo anadza kwa Iye.


Ndipo pamene padatha ngati masiku asanu ndi atatu atanena mau amenewa, Iye anatenga Petro ndi Yohane ndi Yakobo apite naye, nakwera m'phiri kukapemphera.


Pamenepo Yesu, pozindikira kuti alikufuna kudza kudzamgwira Iye, kuti amlonge ufumu, anachokanso kunka kuphiri pa yekha.