Marko 3:13 - Buku Lopatulika13 Ndipo anakwera m'phiri, nadziitanira iwo amene anawafuna Iye mwini; ndipo anadza kwa Iye. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201413 Ndipo anakwera m'phiri, nadziitanira iwo amene anawafuna Iye mwini; ndipo anadza kwa Iye. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa13 Yesu adakwera ku phiri, ndipo adaitana anthu amene Iye mwini ankaŵafuna, iwo nkupitadi kumene kunali Iyeko. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero13 Yesu anakwera ku phiri ndipo anayitana amene anawafuna, ndipo anabwera kwa Iye. Onani mutuwo |