Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Marko 3:12 - Buku Lopatulika

12 Ndipo anailimbitsira mau kuti isamuulule Iye.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

12 Ndipo anailimbitsira mau kuti isamuulule Iye.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

12 Koma Iye ankailetsa mwamphamvu kuti isamuulule.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

12 Koma anayichenjeza mwamphamvu kuti isanene kuti Iye anali ndani.

Onani mutuwo Koperani




Marko 3:12
6 Mawu Ofanana  

nawalimbitsira mau kuti asamuwulule Iye;


Ndipo Yesu ananena naye, Ona, iwe, usauze munthu; koma muka, udzionetse wekha kwa wansembe, nupereke mtulo umene anaulamulira Mose, ukhale mboni kwa iwo.


Ndipo maso ao anaphenyuka. Ndipo Yesu anawauzitsa iwo, nanena, Yang'anirani, asadziwe munthu aliyense.


Ndipo Yesu anaudzudzula, kuti, Khala uli chete, nutuluke mwa iye.


Ndipo anachiritsa anthu ambiri akudwala nthenda za mitundumitundu, natulutsa ziwanda zambiri; ndipo sanalole ziwandazo zilankhule, chifukwa zinamdziwa Iye.


Ndipo anachita chotero masiku ambiri. Koma Paulo anavutika mtima ndithu, nacheuka, nati kwa mzimuwo, Ndikulamulira iwe m'dzina la Yesu Khristu, tuluka mwa iye. Ndipo unatuluka nthawi yomweyo.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa