Yohane 6:15 - Buku Lopatulika15 Pamenepo Yesu, pozindikira kuti alikufuna kudza kudzamgwira Iye, kuti amlonge ufumu, anachokanso kunka kuphiri pa yekha. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201415 Pamenepo Yesu, pozindikira kuti alikufuna kudza kudzamgwira Iye, kuti amlonge ufumu, anachokanso kunka kuphiri pa yekha. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa15 Yesu adaadziŵa kuti anthuwo ankati adzamgwire ndi kumlonga ufumu. Motero adaŵachokera nakakweranso m'phiri payekha. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero15 Yesu atadziwa kuti iwo amafuna kubwera kudzamuwumiriza kuti akhale mfumu, anachoka napita ku phiri pa yekha. Onani mutuwo |