Mateyu 15:29 - Buku Lopatulika29 Ndipo Yesu anachoka kumeneko, nadza kunyanja ya Galileya, nakwera m'phiri, nakhala pansi pamenepo. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201429 Ndipo Yesu anachoka kumeneko, nadza kunyanja ya Galileya, nakwera m'phiri, nakhala pansi pamenepo. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa29 Pambuyo pake Yesu adachoka kumeneko, nayenda m'mbali mwa nyanja ya Galileya. Kenaka adakwera m'phiri nakakhala pansi kumeneko. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero29 Yesu anachoka kumeneko napita mʼmbali mwa nyanja ya Galileya. Ndipo anakwera ku phiri nakhala pansi. Onani mutuwo |