Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Mateyu 15:30 - Buku Lopatulika

30 Ndipo makamu ambiri a anthu anadza kwa Iye, ali nao opunduka miyendo, akhungu, osalankhula, opunduka ziwalo, ndi ena ambiri, nawakhazika pansi pa mapazi ake: ndipo Iye anawachiritsa;

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

30 Ndipo makamu ambiri a anthu anadza kwa Iye, ali nao opunduka miyendo, akhungu, osalankhula, opunduka ziwalo, ndi ena ambiri, nawakhazika pansi pa mapazi ake: ndipo Iye anawachiritsa;

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

30 Anthu ambirimbiri adadza kwa Iye ndi anthu opunduka miyendo, akhungu, olumala, osalankhula, ndiponso ndi odwala ena ambiri. Adaŵakhazika pafupi ndi Yesu, Iye nkuŵachiritsa.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

30 Gulu lalikulu la anthu linabwera kwa Iye ndi anthu olumala, osaona, ofa ziwalo, osayankhula ndi ena ambiri nawagoneka pa mapazi ake ndipo Iye anawachiritsa.

Onani mutuwo Koperani




Mateyu 15:30
14 Mawu Ofanana  

Amene akhululukira mphulupulu zako zonse; nachiritsa nthenda zako zonse;


Ndipo ngati dzanja lako likulakwitsa iwe, ulidule: nkwabwino kwa iwe kulowa m'moyo wopunduka dzanja, koposa kukhala ndi manja ako awiri ndi kulowa mu Gehena, m'moto wosazima.


Koma pamene ukonza phwando uitane aumphawi, opunduka, otsimphina, akhungu;


Amuna inu Aisraele, mverani mau awa: Yesu Mnazarayo, mwamuna wochokera kwa Mulungu, wosonyezedwa kwa inu ndi zimphamvu, ndi zozizwa, ndi zizindikiro, zimene Mulungu anazichita mwa Iye pakati pa inu monga mudziwa nokha;


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa