Yohane 6:2 - Buku Lopatulika2 Ndipo khamu lalikulu la anthu linamtsata Iye, chifukwa anaona zizindikiro zimene anachita pa odwala. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20142 Ndipo khamu lalikulu la anthu linamtsata Iye, chifukwa anaona zizindikiro zimene anachita pa odwala. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa2 Khamu lalikulu la anthu lidamtsatira, chifukwa lidaaona zizindikiro zozizwitsa zimene adaachita pakuchiritsa anthu odwala. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero2 ndipo gulu lalikulu la anthu linamutsata Iye chifukwa linaona zizindikiro zodabwitsa zimene anazichita pa odwala. Onani mutuwo |