Yohane 6:3 - Buku Lopatulika3 Koma Yesu anakwera kuphiri, nakhala pansi komweko pamodzi ndi ophunzira ake. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20143 Koma Yesu anakwera kuphiri, nakhala pansi komweko pamodzi ndi ophunzira ake. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa3 Yesu adakwera m'phiri nakhala pansi ndi ophunzira ake. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero3 Kenaka Yesu anakwera pa phiri nakhala pansi ndi ophunzira ake. Onani mutuwo |