Yohane 6:4 - Buku Lopatulika4 Ndipo Paska, chikondwerero cha Ayuda, anayandikira. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20144 Ndipo Paska, chikondwerero cha Ayuda, anayandikira. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa4 Chikondwerero chija chachipembedzo chotchedwa Paska chidaayandikira. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero4 Tsopano phwando la Paska la Ayuda linali pafupi. Onani mutuwo |