Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Yohane 6:4 - Buku Lopatulika

4 Ndipo Paska, chikondwerero cha Ayuda, anayandikira.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

4 Ndipo Paska, chikondwerero cha Ayuda, anayandikira.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

4 Chikondwerero chija chachipembedzo chotchedwa Paska chidaayandikira.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

4 Tsopano phwando la Paska la Ayuda linali pafupi.

Onani mutuwo Koperani




Yohane 6:4
9 Mawu Ofanana  

Mwezi woyamba, tsiku lakhumi ndi chinai la mweziwo, madzulo, pali Paska wa Yehova.


Tsiku lake loyamba mukhale nao msonkhano wopatulika; musamagwira ntchito ya masiku ena.


Koma Paska wa Ayuda anali pafupi; ndipo ambiri anakwera kunka ku Yerusalemu kuchoka kuminda, asanafike Paska, kukadziyeretsa iwo okha.


Pomwepo anatsala masiku asanu ndi limodzi asanafike Paska, Yesu anadza ku Betaniya kumene kunali Lazaro, amene Yesu adamuukitsa kwa akufa.


Koma pasanafike chikondwerero la Paska, Yesu, podziwa kuti nthawi yake idadza yakuchoka kutuluka m'dziko lino lapansi, kunka kwa Atate, m'mene anakonda ake a Iye yekha a m'dziko lapansi, anawakonda kufikira chimaliziro.


Ndipo Paska wa Ayuda unayandikira, ndipo Yesu anakwera kunka ku Yerusalemu.


Zitapita izi panali chikondwerero cha Ayuda; ndipo Yesu anakwera kunka ku Yerusalemu.


Samalirani mwezi wa Abibu, kuti muzichitira Yehova Mulungu wanu Paska; popeza m'mwezi wa Abibu Yehova Mulungu wanu anakutulutsani m'dziko la Ejipito usiku.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa