Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Yohane 2:5 - Buku Lopatulika

Amake ananena kwa atumiki, Chimene chilichonse akanena kwa inu, chitani.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Amake ananena kwa atumiki, Chimene chilichonse akanena kwa inu, chitani.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Apo amai ake adauza anyamata amene ankatumikira kuti, “Chilichonse chimene akuuzeni, muchite.”

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Amayi ake anati kwa antchito, “Inu muchite chilichonse chimene akuwuzeni.”

Onani mutuwo



Yohane 2:5
12 Mawu Ofanana  

Ndipo pamene dziko lonse la Ejipito linali ndi njala, anthu anafuulira Farao awapatse chakudya; ndipo Farao anati kwa Aejipito onse, Pitani kwa Yosefe: chimene iye anena kwa inu chitani.


Chotero anachita Nowa, monga mwa zonse anamlamulira iye Mulungu, momwemo anachita.


Ndipo ndinachita monga momwe anandilamulira, ndinatulutsa akatundu anga usana, ngati a pa ulendo wa kundende, ndi madzulo ndinaboola pakhoma ndi dzanja langa, ndinawatulutsa pali mdima, ndi kuwasenza paphewa panga pamaso pao.


Pamene Iye anali chilankhulire ndi makamu, onani, amake ndi abale ake anaima panja, nafuna kulankhula naye.


Muli abwenzi anga inu, ngati muzichita zimene ndikulamulani inu.


komatu, uka, nulowe m'mzinda, ndipo kudzanenedwa kwa iwe chimene uyenera kuchita.


Ndi chikhulupiriro Abrahamu, poitanidwa, anamvera kutuluka kunka kumalo amene adzalandira ngati cholowa; ndipo anatuluka wosadziwa kumene akamukako.


ndipo pamene anakonzeka wamphumphu anakhala kwa onse akumvera Iye chifukwa cha chipulumutso chosatha;


Chilichonse chichokera kumpesa asadyeko, asamwe vinyo kapena choledzeretsa, kapena kudya chilichonse chodetsa; zonse ndinamlamulira azisunge.


Pamenepo anatsikira popunthirapo, nachita zonse monga umo mpongozi wake adamuuza.