Mateyu 12:46 - Buku Lopatulika46 Pamene Iye anali chilankhulire ndi makamu, onani, amake ndi abale ake anaima panja, nafuna kulankhula naye. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201446 Pamene Iye anali chilankhulire ndi makamu, onani, amake ndi abale ake anaima panja, nafuna kulankhula naye. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa46 Pamene Yesu ankalankhula ndi anthu ambirimbiri aja, nthaŵi yomweyo amai ake ndi abale ake adafika, naima panja. Ankafuna mpata woti alankhule naye. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero46 Pamene Yesu anali kuyankhulabe ndi gulu la anthu, amayi ndi abale ake anayimirira kunja, akufuna kuyankhulana naye. Onani mutuwo |