Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Yohane 11:5 - Buku Lopatulika

Koma Yesu anakonda Marita, ndi mbale wake, ndi Lazaro.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Koma Yesu anakonda Marita, ndi mbale wake, ndi Lazaro.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Ndiye kuti Yesu ankakonda Marita ndi mng'ono wake Maria ndiponso Lazaro.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Yesu anakonda Marita, mchemwali wake ndi Lazaro.

Onani mutuwo



Yohane 11:5
11 Mawu Ofanana  

Ndipo pakupita paulendo pao Iye analowa m'mudzi wina; ndipo mkazi wina dzina lake Marita anamlandira Iye kunyumba kwake.


Koma Marita anatekeseka ndi kutumikira kwambiri; ndipo anadzako nati, Ambuye, kodi simusamala kuti mbale wanga anandisiya nditumikire ndekha? Mumuuze tsono kuti andithandize.


Koma Ambuye anayankha nati kwa iye, Marita, Marita, uda nkhawa nuvutika ndi zinthu zambiri;


Koma panali munthu wodwala, Lazaro wa ku Betaniya, wa m'mudzi wa Maria ndi mbale wake Marita.


Pamenepo alongo ake anatumiza kwa Iye, nanena, Ambuye, onani, amene mumkonda adwala.


Chifukwa chake Ayuda ananena, Taonani, anamkondadi!


Chifukwa chake pamene anamva kuti anadwala, anakhala pamenepo pamalo pomwepo masiku awiri.


Ophunzira ananena ndi Iye, Rabi, Ayuda analikufuna kukuponyani miyala tsopano apa; ndipo munkanso komweko kodi?


pakuti Atate yekha akonda inu, chifukwa inu mwandikonda Ine, ndi kukhulupirira kuti Ine ndinatuluka kwa Atate.


ndipo ndinazindikiritsa iwo dzina lanu, ndipo ndidzalizindikiritsa; kuti chikondi chimene munandikonda nacho chikhale mwa iwo, ndi Ine mwa iwo.