Luka 10:41 - Buku Lopatulika41 Koma Ambuye anayankha nati kwa iye, Marita, Marita, uda nkhawa nuvutika ndi zinthu zambiri; Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201441 Koma Ambuye anayankha nati kwa iye, Marita, Marita, uda nkhawa nuvutika ndi zinthu zambiri; Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa41 Ambuye adati, “Iwe Marita iwe, ukutekeseka nkuvutika ndi zinthu zambiri, Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero41 Ambuye anati, “Marita, Marita, ukudandaula ndi kuvutika ndi zinthu zambiri, Onani mutuwo |