Luka 10:42 - Buku Lopatulika42 koma chisoweka chinthu chimodzi, pakuti Maria anasankha dera lokoma limene silidzachotsedwa kwa iye. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201442 koma chisoweka chinthu chimodzi, pakuti Maria anasankha dera lokoma limene silidzachotsedwa kwa iye. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa42 koma chofunika nchimodzi chokha. Maria ndiye wasankhula chinthu chopambana, ndipo chimenechi palibe wina angamlande ai.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero42 koma chofunika nʼchimodzi chokha. Mariya wasankha chinthu chabwino, ndipo palibe angamulande chimenechi.” Onani mutuwo |