Yohane 11:6 - Buku Lopatulika6 Chifukwa chake pamene anamva kuti anadwala, anakhala pamenepo pamalo pomwepo masiku awiri. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20146 Chifukwa chake pamene anamva kuti anadwala, anakhala pamenepo pa malo pomwepo masiku awiri. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa6 Komabe pamene adamva za matendawo, Yesu adaswera masiku aŵiri pamalo pomwe adaaliripo. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero6 Koma atamva kuti Lazaro akudwala, Iye anakhalabe kumene anali masiku ena awiri. Onani mutuwo |