Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Yohane 11:7 - Buku Lopatulika

7 Ndipo pambuyo pake ananena kwa ophunzira ake, Tiyeni tipitenso ku Yudeya.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

7 Ndipo pambuyo pake ananena kwa ophunzira ake, Tiyeni tipitenso ku Yudeya.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

7 Pambuyo pake adauza ophunzira ake kuti, “Tiyeni tipitenso ku Yudeya.”

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

7 Kenaka anati kwa ophunzira ake, “Tiyeni tibwerere ku Yudeya.”

Onani mutuwo Koperani




Yohane 11:7
6 Mawu Ofanana  

Ndipo pa kubadwa kwake kwa Yesu mu Betelehemu wa Yudeya m'masiku a Herode mfumu, onani, Anzeru a kum'mawa anafika ku Yerusalemu,


Ndipo panali, pamene anayamba kukwanira masiku akuti alandiridwe Iye kumwamba, Yesu anatsimikiza kuloza nkhope yake kunka ku Yerusalemu,


Chifukwa chake pamene anamva kuti anadwala, anakhala pamenepo pamalo pomwepo masiku awiri.


Patapita masiku, Paulo anati kwa Barnabasi, Tibwerere, tizonde abale m'mizinda yonse m'mene tinalalikiramo mau a Ambuye, tione mkhalidwe wao.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa