Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Yohane 11:36 - Buku Lopatulika

36 Chifukwa chake Ayuda ananena, Taonani, anamkondadi!

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

36 Chifukwa chake Ayuda ananena, Taonani, anamkondadi!

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

36 Pamenepo anthu aja adati, “Onani, ankamukonda zedi.”

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

36 Pamenepo Ayuda anati, “Taonani mmene Iye anamukondera Lazaro!”

Onani mutuwo Koperani




Yohane 11:36
10 Mawu Ofanana  

koma ambiri a mwa Ayuda adadza kwa Marita ndi Maria, kudzawatonthoza mtima pa mlongo wao.


Pamenepo alongo ake anatumiza kwa Iye, nanena, Ambuye, onani, amene mumkonda adwala.


ndipo yendani m'chikondi monganso Khristu anakukondani inu, nadzipereka yekha m'malo mwathu, chopereka ndi nsembe kwa Mulungu, ikhale fungo lonunkhira bwino.


Amuna inu, kondani akazi anu, monganso Khristu anakonda Mpingo, nadzipereka yekha m'malo mwake;


Taonani, chikondicho Atate watipatsa, kuti titchedwe ana a Mulungu; ndipo tili ife otere. Mwa ichi dziko lapansi silizindikira ife, popeza silimzindikira Iye.


ndi kwa Yesu Khristu, mboni yokhulupirikayo, wobadwa woyamba wa akufa, ndi mkulu wa mafumu a dziko lapansi. Kwa Iye amene atikonda ife, natimasula kumachimo athu ndi mwazi wake;


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa