Yohane 11:37 - Buku Lopatulika37 Koma ena mwa iwo anati, Kodi uyu wotsegulira maso wosaona uja, sakanatha kodi kuchita kuti asafe ameneyunso? Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201437 Koma ena mwa iwo anati, Kodi uyu wotsegulira maso wosaona uja, sanakhoza kodi kuchita kuti sakadafa ameneyunso? Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa37 Koma ena mwa iwo adati, “Munthu uyu suja adapenyetsa munthu wosapenya uja? Monga sakadatha kuchitapo kanthu kuti Lazaroyu asafe?” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero37 Koma ena a iwo anati, “Iye amatsekula maso a munthu wosaona, kodi sakanakhoza kuletsa kuti munthu uyu asamwalire?” Onani mutuwo |