Yohane 16:27 - Buku Lopatulika27 pakuti Atate yekha akonda inu, chifukwa inu mwandikonda Ine, ndi kukhulupirira kuti Ine ndinatuluka kwa Atate. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201427 pakuti Atate yekha akonda inu, chifukwa inu mwandikonda Ine, ndi kukhulupirira kuti Ine ndinatuluka kwa Atate. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa27 pakuti okukondani ndi Atate amene. Amakukondani chifukwa mumandikonda, ndipo mumakhulupirira kuti ndidachokera kwa Iwo. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero27 Atate mwini anakukondani chifukwa inu mwandikonda Ine ndipo mwakhulupirira kuti Ine ndinabwera kuchokera kwa Atate. Onani mutuwo |