Yohane 11:3 - Buku Lopatulika3 Pamenepo alongo ake anatumiza kwa Iye, nanena, Ambuye, onani, amene mumkonda adwala. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20143 Pamenepo alongo ake anatumiza kwa Iye, nanena, Ambuye, onani, amene mumkonda adwala. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa3 Tsono alongo ake aja adatumiza thenga kwa Yesu kukamuuza kuti, “Ambuye, bwenzi lanu uja akudwala.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero3 Choncho alongo ake anatumiza mawu kwa Yesu kuti, “Ambuye, uja amene Inu mumamukonda akudwala.” Onani mutuwo |