Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Numeri 25:9 - Buku Lopatulika

Ndipo akufa nao mliri ndiwo zikwi makumi awiri ndi zinai.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Ndipo akufa nao mliri ndiwo zikwi makumi awiri ndi zinai.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Komabe anthu okwanira 24,000 anali atafa kale ndi mliriwo.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Pa mliriwo, anthu okwana 24,000 anafa.

Onani mutuwo



Numeri 25:9
11 Mawu Ofanana  

Chomwecho Yehova anatumiza mliri pa Israele kuyambira m'mawa kufikira nthawi yoikika; ndipo anafapo anthu zikwi makumi asanu ndi awiri kuyambira ku Dani kufikira ku Beereseba.


Ndipo Yehova anakantha anthu, chifukwa anapanga mwanawang'ombe amene Aroni anapanga.


amuna amene anaipsa mbiri ya dziko, anafa ndi mliri pamaso pa Yehova.


Ndipo anaima pakati pa akufa ndi amoyo; ndi mliri unaleka.


Ndipo Yehova ananena ndi Mose, nati,


Ndipo kunali, utatha mliriwo, Yehova ananena ndi Mose ndi Eleazara mwana wa Aroni wansembe, nati,


Taonani, awa analakwitsa ana a Israele pa Yehova ndi cha Peori chija, monga adawapangira Balamu; kotero kuti kunali mliri m'khamu la Yehova.


Kapena tisachite dama monga ena a iwo anachita dama, nagwa tsiku limodzi zikwi makumi awiri ndi zitatu.