Numeri 14:37 - Buku Lopatulika37 amuna amene anaipsa mbiri ya dziko, anafa ndi mliri pamaso pa Yehova. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201437 amuna amene anaipsa mbiri ya dziko, anafa ndi mliri pamaso pa Yehova. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa37 Anthu onsewo amene ankasimba zoipa za dzikolo, adafa ndi mliri pamaso pa Chauta. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero37 Anthu amene ankafalitsa mbiri yoyipa ya dzikolo anakanthidwa ndi mliri ndipo anafa pamaso pa Yehova. Onani mutuwo |