Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Numeri 14:38 - Buku Lopatulika

38 Koma Yoswa mwana wa Nuni, ndi Kalebe mwana wa Yefune, anakhala ndi moyo mwa amuna aja adamukawo kukazonda dziko.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

38 Koma Yoswa mwana wa Nuni, ndi Kalebe mwana wa Yefune, anakhala ndi moyo mwa amuna aja adamukawo kukazonda dziko.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

38 Koma mwa anthu amene adapita kukazonda dziko aja, Yoswa mwana wa Nuni ndi Kalebe mwana wa Yefune ndiwo adatsala amoyo.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

38 Mwa anthu amene anakaona dzikolo, Yoswa mwana wa Nuni ndi Kalebe mwana wa Yefune ndi okhawo amene anapulumuka.

Onani mutuwo Koperani




Numeri 14:38
5 Mawu Ofanana  

Wa fuko la Yuda, Kalebe mwana wa Yefune.


amuna amene anaipsa mbiri ya dziko, anafa ndi mliri pamaso pa Yehova.


Ndipo Mose anauza ana a Israele mau onse awa; ndipo anthu anamva chisoni chambiri.


Popeza Yehova adanena za iwowa, Adzafatu m'chipululu. Ndipo sanatsalire mmodzi wa iwowa koma Kalebe mwana wa Yefune, ndi Yoswa mwana wa Nuni.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa