Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Numeri 14:39 - Buku Lopatulika

39 Ndipo Mose anauza ana a Israele mau onse awa; ndipo anthu anamva chisoni chambiri.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

39 Ndipo Mose anauza ana a Israele mau onse awa; ndipo anthu anamva chisoni chambiri.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

39 Mose adaŵafotokozera Aisraele mau onseŵa, ndipo anthu adalira kwambiri.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

39 Mose atafotokoza izi kwa Aisraeli onse, anthuwo analira kwambiri.

Onani mutuwo Koperani




Numeri 14:39
8 Mawu Ofanana  

Ndipo pamene anthu anamva mau awa oipa anachita chisoni; ndipo panalibe mmodzi anavala zokometsera zake.


Utsiru wa munthu ukhotetsa njira yake; mtima wake udandaula pa Yehova.


Yehova, iwo adza kwa Inu movutika, iwo anathira pemphero, muja munalikuwalanga.


Nunene nao, Pali Ine ati Yehova, ndidzachitira inu ndithu monga mwanena m'makutu mwanga;


Koma Yoswa mwana wa Nuni, ndi Kalebe mwana wa Yefune, anakhala ndi moyo mwa amuna aja adamukawo kukazonda dziko.


koma anawo a Ufumu adzatayidwa kumdima wakunja; komweko kudzakhala kulira ndi kukukuta mano.


Pakuti mudziwa kutinso pamene anafuna kulowa dalitsolo, anakanidwa (pakuti sanapeze malo akulapa), angakhale analifunafuna ndi misozi.


Mwa ichi ana a Israele sangathe kuima pamaso pa adani ao, awafulatira adani ao, pakuti aperekedwa aonongeke. Sindidzakhalanso nanu mukapanda kuononga choperekedwacho, kuchichotsa pakati pa inu.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa