Numeri 25:8 - Buku Lopatulika8 natsata munthu Mwisraele m'hema, nawapyoza onse awiri, munthu Mwisraele ndi mkaziyo m'mimba mwake. Pamenepo mliri unaletseka kwa ana a Israele. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20148 natsata munthu Mwisraele m'hema, nawamoza onse awiri, munthu Mwisraele ndi mkaziyo m'mimba mwake. Pamenepo mliri unaletseka kwa ana a Israele. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa8 Ndipo adatsatira Mwisraele uja mpaka kukaloŵa m'chipinda cham'kati, nabaya onse aŵiriwo, Mwisraeleyo pamodzi ndi mkaziyo. Motero mliri udaleka pakati pa Aisraele. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero8 Ndipo anatsatira Mwisraeliyu mpaka mʼtenti yake. Anasolola mkondowo ndi kubaya awiriwo kupyola Mwisraeliyo mpaka mʼthupi la mkaziyo. Pamenepo mliri unaleka pakati pa Aisraeli. Onani mutuwo |