Numeri 25:7 - Buku Lopatulika7 Pamene Finehasi mwana wa Eleazara, mwana wa Aroni wansembe, anachiona, anauka pakati pa khamu, natenga nthungo m'dzanja lake; Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20147 Pamene Finehasi mwana wa Eleazara, mwana wa Aroni wansembe, anachiona, anauka pakati pa khamu, natenga nthungo m'dzanja lake; Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa7 Finehasi mwana wa Eleazara, mdzukulu wa Aroni, ataona zimenezo, adadzuka nasiya mpingowo, nakatenga mkondo. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero7 Finehasi mwana wa Eliezara, mwana wa wansembe Aaroni ataona izi, anachoka pa msonkhanowo, natenga mkondo mʼdzanja lake. Onani mutuwo |