Numeri 25:6 - Buku Lopatulika6 Ndipo, taonani, anadza wina wa ana a Israele, nabwera naye mkazi Mmidiyani kudza naye kwa abale ake, pamaso pa Mose, ndi pamaso pa khamu lonse la ana a Israele, pakulira iwo pa khomo la chihema chokomanako. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20146 Ndipo, taonani, anadza wina wa ana a Israele, nabwera naye mkazi Mmidiyani kudza naye kwa abale ake, pamaso pa Mose, ndi pamaso pa khamu lonse la ana a Israele, pakulira iwo pa khomo la chihema chokomanako. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa6 Tsono Mwisraele wina adabwera ndi mkazi Wachimidiyani kubanja kwake, Mose ndi Aisraele onse akupenya, pamene ankalira pakhomo pa chihema chamsonkhano. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero6 Kenaka mwamuna wina wa ku Israeli anabweretsa ku banja lake mkazi wa Chimidiyani pamaso pa Mose ndi anthu onse a Israeli pamene ankalira pa khomo la tenti ya msonkhano. Onani mutuwo |