Numeri 25:9 - Buku Lopatulika9 Ndipo akufa nao mliri ndiwo zikwi makumi awiri ndi zinai. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20149 Ndipo akufa nao mliri ndiwo zikwi makumi awiri ndi zinai. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa9 Komabe anthu okwanira 24,000 anali atafa kale ndi mliriwo. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero9 Pa mliriwo, anthu okwana 24,000 anafa. Onani mutuwo |