Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Numeri 26:1 - Buku Lopatulika

1 Ndipo kunali, utatha mliriwo, Yehova ananena ndi Mose ndi Eleazara mwana wa Aroni wansembe, nati,

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

1 Ndipo kunali, utatha mliriwo, Yehova ananena ndi Mose ndi Eleazara mwana wa Aroni wansembe, nati,

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

1 Utatha mliriwo, Chauta adauza Mose ndi Eleazara, mwana wa wansembe Aroni, kuti,

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

1 Utatha mliri Yehova anati kwa Mose ndi Eliezara mwana wa Aaroni,

Onani mutuwo Koperani




Numeri 26:1
3 Mawu Ofanana  

Monga Yehova analamula Mose, momwemo anawawerenga m'chipululu cha Sinai.


popeza akusautsani ndi manyengo ao amene anakunyengani nao; m'chija cha Peori, ndi cha Kozibi, mwana wamkazi wa kalonga wa ku Midiyani, mlongo wao, amene adamupha tsiku la mliri, m'chija cha Peori.


Ndipo akufa nao mliri ndiwo zikwi makumi awiri ndi zinai.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa