Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Numeri 24:22 - Buku Lopatulika

Koma Kaini adzaonongeka, kufikira Asiriya adzakumanga nsinga.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Koma Kaini adzaonongeka, kufikira Asiriya adzakumanga nsinga.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

komabe mudzaonongeka inu ana a Kaini, mudzakhala mu ukapolo wa Asuri nthaŵi yaitali.”

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

komabe inu Akeni mudzawonongedwa, pamene Asuri adzakutengeni ukapolo.”

Onani mutuwo



Numeri 24:22
8 Mawu Ofanana  

M'dziko momwemo iye anatuluka kunka ku Asiriya, namanga Ninive, ndi mzinda wa Rehoboti, ndi Kala,


Ndiponso kwa Semu atate wa ana onse a Eberi, mkulu wa Yafeti, kwa iye kunabadwa ana.


Ana aamuna a Semu; Elamu, ndi Asiriya, ndi Aripakisadi, ndi Ludi, ndi Aramu.


Akeni ndi Akenizi, Akadimoni,


anayandikira kwa Zerubabele, ndi kwa akulu a nyumba za makolo, nanena nao, Timange pamodzi nanu; pakuti timfuna Mulungu wanu monga inu, ndipo timamphera nsembe chiyambire masiku a Esarahadoni mfumu ya Asiriya, amene anatikweretsa kuno.


Asiriya anaphatikana nao; anakhala dzanja la ana a Loti.


Asiriya sadzatipulumutsa; sitidzayenda pa akavalo, ndipo sitidzanenanso kwa ntchito ya manja athu, Inu ndinu milungu yathu; pakuti mwa Inu ana amasiye apeza chifundo.


Ndipo ananena fanizo lake, nati, Ha! Adzakhala ndi moyo ndani pakuchita ichi Mulungu?