Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Genesis 10:21 - Buku Lopatulika

21 Ndiponso kwa Semu atate wa ana onse a Eberi, mkulu wa Yafeti, kwa iye kunabadwa ana.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

21 Ndiponso kwa Semu atate wa ana onse a Eberi, mkulu wa Yafeti, kwa iye kunabadwa ana.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

21 Semu ndiye kholo la ana onse a Eberi, ndiponso ndiye mkulu wake wa Yafeti. Iyeyu anali ndi ana.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

21 Semu amene anali mkulu wake wa Yafeti nayenso anabereka nakhala kholo la Eberi.

Onani mutuwo Koperani




Genesis 10:21
7 Mawu Ofanana  

Amenewa ndi ana aamuna a Hamu monga mwa mabanja ao, mwa zinenedwe zao, m'maiko ao, m'mitundu yao.


Ana aamuna a Semu; Elamu, ndi Asiriya, ndi Aripakisadi, ndi Ludi, ndi Aramu.


Ndipo Nowa anali wa zaka mazana asanu; ndipo Nowa anabala Semu ndi Hamu ndi Yafeti.


Ana a Semu: Elamu, ndi Asiriya, ndi Aripakisadi, ndi Ludi, ndi Aramu, ndi Uzi, ndi Huli, ndi Getere, ndi Meseki.


Koma Kaini adzaonongeka, kufikira Asiriya adzakumanga nsinga.


Koma zombo zidzafika kuchokera ku dooko la Kitimu, ndipo adzasautsa Asiriya, nadzasautsa Eberi, koma iyenso adzaonongeka.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa